Driemo kupanga zibwana atisiya ngati pop young soon😂
Violence Academy FM
Contact information, map and directions, contact form, opening hours, services, ratings, photos, videos and announcements from Violence Academy FM, Box 6678, Lilongwe.
Welcome to �*Violence Acadamy�
This is online Radio station
Yomwe timakhala tikupanga ma interview ma artist osiyana siyana
Ma big artist komaso ma upcoming artists��
02/01/2024
uthenga ndumenewu
10/10/2023
Spy-Kay 98
Nthawi nka kape
Osamada nkhawa muli okuda kale
Kell Kay
Tiyeni uku gyz..
Tikadumphe
BASI PACHIYAMBI MULUNGU ADALENGA INUYO
UBWINO KU MWAMBA ALIYESE AKAKHALA NTUNDU WAKE WENI WENI 😯😯😯
Kunali Gaffah pano Ali kuti?
Kunali 2kings Mhsrip
Kunali Gray matter pano Ali kuti?
Kunali kandapako empire pano akungogulisa chimanga cha anthu ku madimbaku
Kunali lay one pano Ali ku jowen plan alibe
Kunali G paper pano Ali mu lilongwemu ndi dzamba kwa azising'anga aponye comment wa
Kunali ice kid pano nde ndi uyu amavala zofila amagulisa samusa ku Airtel komaso ati ndi ujen.
Kunali Spy k pano nde ulovi wamudyatu ku lifuu ko
Kunali Sheri b awawa nde sankatha kuimba
Kunali Mr love pano anapenga atakhala dzaka zambili asakutchuka
Kunali Tiyo uyuyu nde khalidwe la ice kid lijatu basi
Dear upcoming artists anthu onsewa alembedwawa anatha
Mashasha ndinuyo mukumveka panonu
Nyimbo zomwe amati anayimba bwinozo ndi zomwe zomwezo
Za 2014 zija
Ma producer nonse mupite kwa olusa akakupaseni ma tutorials
Zikomo
ICE KID ATENGELA KAY-DO MAFIA KU BWALO LA MILANDU
Precious chirwa yemwe amadziwika ndi dzina loti ice kid lero watengera oyimba wina wa chamba cha dancehall mu Boma la salima otchuka ndi dzina loti Kay do mafia ku bwalo la milandu mu Boma lomwero la salima.
Ma report omwe angotipeza kumene akuti ice kid masana a tsiku la chisano anapita pa tsamba la mchedzo(Facebook) nkuyamba kumunyoza Kay do mafia kuti si kadaulo kunkhani ya mayimbidwe,poonjezela Apo ice kid analembaso mawu ena onyoza oyimba winaso odziwika ndi dzina loti Mo B Malawi.
Ice kid ataona kuti sanawayankhulire bwino oyimba anzakewa iyeyu anabwelaso pa tsamba la tchezo lomwero napepesa koma motsindikabe kuti katswili oyimba chamba cha chambayu(Kay do mafia) sathabe kuimba ndipo aphudzile,
Mu mawu ake iye anatamanda oyimba ena amu Boma lomweri kuti ndi anamandwa ku nkhani ya maimbidwe,.
Izi sizinasangalase oyimba wa chamba cha chambayu (Kay do) ndipo iye posonyeza nkwiyo wake anabwelaso poyela kuzaulura za mchitidwe wa kathyali oyimba nyimbo zodikulazi ice kid kuti ndi mgotchana(anyamata ochita mchitidwe ogonana okha okha) zomwe zinaphyesa ntima ice kid kuti afike pomutengera kay do mafia ku BWALO la milandu la salima magistrate court.
Tikudikila chigamuro kuchokera ku bwalo laza milandu
Munali ndi ine muulusi wanu Nkaladi
Komano wats fridge in chichewa?
Click here to claim your Sponsored Listing.
Location
Contact the school
Telephone
Website
Address
Lilongwe