03/05/2026
mdalitso wina ukukusemphano chifukwa cha aja mudawakwiira aja, tawakhululukiran muone chikondi cha mulungu lero
Happy Sunday🥳
Poet and Chinese student
03/05/2026
mdalitso wina ukukusemphano chifukwa cha aja mudawakwiira aja, tawakhululukiran muone chikondi cha mulungu lero
Happy Sunday🥳
02/05/2026
nanga momwe wavutira Malawi basi wina azidulitsa phon nanga munda🤣
kutengeka, kufuna kufanana level ndi a nebor zotsaitira zake ndi zimenezo 🤣🤣
02/05/2026
Album yomwe Mlakatuli Raphael Sitima akutulutsa mawa, only Autice mdzuma the poet featured one of his poem . tiyeni tikumane ku lilongwe CCAP hall mawa laliwisili tikayapatse motsooo🥳🥳🥳🥳
Nthawi ya moyo zochitika ndizambiri.
ngati wakuswani mtima ndiye kuti muli mu nthawi ya moyo. open new chapter 😎
01/05/2026
The staaaaaaaageeee master Raphael sitima ali ndi show kuseli kwa mawa uku, kulalikira walalikira koma tsiku ili ndilomaliza, tiyeeeeenni tonse tikakumane ku lilongwe CCAP hall kodi inu zabwino ayiiiiii???🥳🥳🥳
01/05/2026
LISTEN TO MY STORY ON LABOURS DAY 🙏🙏🙏🙏🙏🙏😭😭
I was born into a poor family of eight children in a rural village, life was never easy. We could not always afford proper clothes or even a good meal, but the desire to learn never left me.
I started primary school at the age of 8, later went on to Dowa Secondary School, and by God’s grace, I passed my MSCE becoming the only person in my entire village to achieve it. That moment changed everything.
I continued my journey at Kasungu Teachers Training College, and in 2018, I began my career as a professional teacher. But I didn’t stop there.
In 2024, I took another bold step and enrolled at MUST to study a Bachelor of Arts in Languages and Communication, specializing in Chinese and English.
Looking back, I see not just struggle, but strength. Not just lack, but determination. And above all, God’s hand guiding me every step of the way.
I thank God for this journey 🙏🙏🙏
Happy labours day
from inbox
"I am 30yrs man, am looking for FAIRY used woman of about 25-28 yrs"
30/04/2026
Alamu anu akuchimuna abwera ndi mwana kwanu, akukuuzani kuti musamuletse amalira. ladies let's goo🤣
30/04/2026
ena simundidzwa koma mukachita search pa Google ikupatsani information yonse, osaiwala tili ndi album launch ya Raphael sitima ku lilongwe pa 3 May. lets cast our last tickets now.
palia tickets awiri a show ya Raphael ndipereka kwa amene comment yake sikhala ndi like
tchulani ubwino umodz okhala single😂
29/04/2026
malinga mkudula kwa fuel, ku Dowa stikupanga nawo zibwana😂